OG Issah joins Zomba Changalume parliamentary by-elections

A popular Blantyre-based businessman OG Issah has joined the Zomba Changalume parliamentary race.

OG Issa

Mahomed Hanif Osman popularly known as ‘OG Issa’ is upbeat that he will win yhe parliamentary seat.

Reports say Osman will stand as an independent candidate and will contest  with other  candidates standing on PP, UTM, DPP and UDF tickets.

Osman was 2014-2019 legislator  for Chiradzulu Central Constituency.

Malawi Congress Party is not featuring any candidate but will support one of the candidates.

Zomba Changalume Parliamentary seat fell vacant after the death of legislator John Chikalimba who was also leader for PP in the National Assembly.

Follow and Subscribe Nyasa TV :

Sharing is caring!

Follow us in Twitter
15 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Benjones87
Benjones87
3 years ago

I hope he has not misused his position just to a aquire land in chiradzulu.

Alufa
Alufa
3 years ago

Palibe chomwe munatipangira Ku chiradzulu central kuno, musapeperetsenso ena boss

mtete
mtete
3 years ago

At least this one votes, not the “dziko ndi wanu ndalama ndi wathu” type. Komabe ndi m’Mwenye basi.

Mwenye
Mwenye
3 years ago
Reply to  mtete

Racist

Ziggy
Ziggy
3 years ago

A ku zomba sife opusa atiuze kwawo

Phudzi
Phudzi
3 years ago

Wachika ku Chiradzulo kukaimira ku Zomba? Moti anthu aku changalume adzikavotera zopusa zimenezi kusiya mbadwa zakonko zoti zikawa thandiza? Anthu amenewa atijaila kobasi, ngakhale mumawa bakira kuti ndi akuno koma olo ntakakhala ku dziko la amwenye mdzukulu wanga sangaka imire u MP. Adya kokwana misonkho yathu

Makayika
Makayika
3 years ago

Koma amwenye atitola kwambiri angoyima kumene akufuna ali pheeee ndiye mmalawi okonda soya pieces atengeka naye basi nane ndikayime ku India koma

Dausee
Dausee
3 years ago

Palibe chimene anapanga ku CZ fans ya ku ZA musapusisike.

Kudya katatu patsiku
Kudya katatu patsiku
3 years ago

Wawina kale uyu

Mulopwana
3 years ago

Kwawo ndi ku Chiladzulo kapena ku Zomba. Anene bwino ameneyu kapen ku Chilazulo ndi kwawo kwa amake.

Prophet
Prophet
3 years ago

Back in the day, we used to go and buy audio cassettes at OG Issa. He was one of the top guys selling audio cassettes and I am 47 now. I am sure a lot of people will remember those days.

zikunka nabeba kwa masharubu
zikunka nabeba kwa masharubu
3 years ago
Reply to  Prophet

…ndipo gulu limeneli la amwenye amakaseti ili linkabera achina Mlaka, Billy Kaunda, Master Tongole,…oyimba onseeee. Mwini luso kutchuka koma wokudya mane n’kukhala OG Issa, mwini luso kumangonyambitira fungo. Ndiye chifukwa chake Matafale anawatopera. Woyimba kufufuza pa ground kupeza kuti almost banja lililonse linagula kaseti ya Nsaku koma Nsaku mwiniwakeyo kulandirako zamakaseti 1000 basi, eeeeh OG Issa ayi ndithu. Ndichifukwa chake wathawano ku Chiradzulo atamuzindikira bodza lake kuti akabodzenso ku Zomba, mwinanso next time adzayimira ku Likoma. Kaya ku Zomba analembetsako bwanji kaya, m’mwenye woti anakhazikika ku Mzedi? Nayo MCP ilibe manyazi kumapangana naye zimenezi mwamseli. That is how desperate MCP… Read more »

Chinyanyailinaise
Chinyanyailinaise
3 years ago
Reply to  Prophet

..and how old is OGI if you are 47 now

Read previous post:
HRDC members receiving threats from Indian investor Chandra More

A stubborn Indian investor Chandra More  who was reported to the Anti-Corruption Bureau (ACB) by Human Rights Defenders Coalition (HRDC) ...

Close