Police arrest DPP security elite over reign of terror

Malawi Police in the southern region have arrested the notorious 14 members of the opposition Democratic Progressive Party (DPP) called Super 16 blamed for atrocities against the then opposition MCP and UTM.

DPP cadets have a history of abductions and killings.

Police spokesperson in the southern region Ramsy Mushani has confirmed the arrest of the 14 who were always armed and led a shadow paramilitary wing of the party during its reign.

“Our officers from Luchenza have indeed arrested them on crimes of assault, theft and malicious damage.

“They will appear in court after we sort them out according to their crimes,” said Mushani.

The suspected notorious DPP thugs are alleged to have torched the UTM vehicle in Mangochi and beat up severely rights activist Billy Mayaya in Blantyre.

Follow and Subscribe Nyasa TV :

Sharing is caring!

Follow us in Twitter
90 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Nepotism
3 years ago

No sympathy for DPP anthu oyipisitsa

U kambuku wa Chakwera wayamba kuonekera

China chake chichitika muno mu Malawi. Ili ndi dziko. Kamuzu Banda ankazunzanso anthu chonchi. What MCP is doing today is exactly what it did in 60s. It arrested all potential political leaders and technically killed all opposition parties such that by 1964, MCP was the only party left and they rulled with a heavy hand until 1994. Everybody lived in fear such that nobody could afford to voice out the ills of government. That scare tactic is the one which they want to use now. Inu simukudabwa kuti anthuwa akumangidwa pa tizifukwa tina tosamveka bwino? Let us remember that MCP… Read more »

Dan
Dan
3 years ago

There is nothing that will happen for as long as they are leaping what they had sown please dont think DPP ndi Boma No. DPP was a party that simply mistook itself as Malawi now they are harvesting what they had sown. We ae strongly behind the arrest to get the truth that has been hidden by DPP for long. Don’t worry you will have your day in court where evidence will be submitted, evaluated and verdict passed and

Madando Tippex
Madando Tippex
3 years ago
Reply to  Dan

I agree entirely with you.

Lego
3 years ago

You are just showing yourself how dull and stupid you are.Who can support those naughty DPP Cadets the way they were doing?Its only you stupid fool.

Madando Tippex
Madando Tippex
3 years ago

What they (MCP, UTM and others in Tonse Aliiance) are doing is what we voted them for. Mumayesa dziko ndi lanu nokha. Ngati mumamva chizungu amati, “how clever or sophisticated you plan evil, somehow the truth will still come out” Those who wronged other must be punished.

Charles Harrison
Charles Harrison
3 years ago

Alangidwe amenewo,anthu oipa,zilombo,sizikuyenera kumakhala ndi anthu mmudzi,ali ndi zilope.nkhani ya kuvulanza/kupha sinkhani yabwino………………….iweyo ukuonetsa kuti mutu wako ndi wobalalika.usaiwale kuti anthu osalakwa ali mmanda ali mmanda pano.nawosotu moyo amaufuna ngati mmene ukupumila iweyomo.iwe wafa ngati.

Charles Harrison
Charles Harrison
3 years ago

withdraw your comment b4 COB to day

Dlaxla
Dlaxla
3 years ago

Mbuli zimenezo amazigwilitsa ntchito a DPP ZIMANGIDWE NDITHU, akaona ngat dpp sidzatuluka mboma Nyekhwe after Nyekhwe musanati mukadalira ma cadets

Asolewewisi
Asolewewisi
3 years ago

Nothing will happen chief. Pano it’s payback time and payback is a bitch. He who lives by the sword will die by the sword. This should be a person kwa aliyense. Osamayerekedwa ngati dziko lino ndi la munthu mmodzi kapena chipani chimodzi. For your own information, kumbali yomanga anthu this is just the beginning… watch this space.

F. B.
F. B.
3 years ago

What dpp planted it’s what they are leaping
This should be the example to tonse alliance
don’t feel you are at comfortable zone.

Umbuli thoo
3 years ago
Reply to  F. B.

What is leaping pedegu iwe??

Nabetha
Nabetha
3 years ago

masiku forty akakwana akwana…….kulipidwa za misonkho chifukwa cho senza lupanga ndi phwitika!!!! oh my word !!!

MTEMBOSUPHWISA
3 years ago

teach them a lesson

MTEMBOSUPHWISA
3 years ago

burn them arrive , conquer them , plun them

Bandung Cincau
Bandung Cincau
3 years ago

Good job! Aone Nyekhwe amenewa! Anthu odzimva komanso a nkhanza!

Masilu ga liwata
3 years ago

Macadet mumayerekedwa mumaganiza dziko ndilanu

Patrick Phiri
Patrick Phiri
3 years ago

Nanga aja anatseka mseu ku Nsundwe ndi ku Mponelavbwanji salumangidwa?

Lego
3 years ago
Reply to  Patrick Phiri

Inu daily makomenti anu amakhala opanda nzeru kaya umbuli umakudzungudzani kaya.What crime did those commit?

GEORGE CHITHONJE
GEORGE CHITHONJE
3 years ago
Reply to  Lego

MBULI NDIWEYO CADET

Masilu ga liwata
3 years ago
Reply to  Lego

ndiwopusa ameneyu sanapite ku school cadet wachabechaeb

Bob Finye
Bob Finye
3 years ago
Reply to  Lego

You are too brute to understand things. Don’t you know that blocking road is a crime?

Lego
3 years ago
Reply to  Bob Finye

Their were demonstrating and its hard to identify who did this.Moreover it was a peace demonstrations.

Madando Tippex
Madando Tippex
3 years ago
Reply to  Bob Finye

Cadet! Balirani chonchi.

Zofu
Zofu
3 years ago
Reply to  Lego

killed the policeman innocently akayakha kwa Mulungu

Lego
3 years ago
Reply to  Zofu

He was killed on the line of duty.Besides,it was a mob justice.

Gobede
Gobede
3 years ago
Reply to  Lego

Mmmmm man simukuzitsata. So pitanu ku police mukafunse kut mwawaangiranji ?

Bob Finye
Bob Finye
3 years ago
Reply to  Patrick Phiri

Inde. Nsundwe Barracks injatidwenso. Mukuwasiyiranji?

Gobede
Gobede
3 years ago
Reply to  Bob Finye

Hahaha!!!!! M’bale msundwe ndi victim wamva?

Dziko ndi wanthu
Dziko ndi wanthu
3 years ago
Reply to  Patrick Phiri

Katsekuleni mlandu nanu. Muona amangidwa.

msundwe
msundwe
3 years ago
Reply to  Patrick Phiri

Ahhhh komanso Boma la DPP ndiye kayatu. Bwanji silinawamange?

Yasser Arafat
3 years ago
Reply to  Patrick Phiri

Anali a nyau nde mwini dambwe ali pa’ State house ka

Dyera
3 years ago

TIKUDIKILA ZOMWE BOMA LA LERO LIMATINAMIZA PA CAMPAIGN TISAMANGAOMVA ZOMANGANA ZANUZO PANGANI ZOTI MUTHANDIZE A MALAWI. kUMANGANI KUTITHANDIZA CHANI IYAAA

Wachiyao
Wachiyao
3 years ago
Reply to  Dyera

Boma likuchita zomwe ife amene tinalivotera tinapangana nalo. Inu omwe munkasapota agogo aja, zanu zomwe mukufuna mukapemphe kwa agogo anu omwewo. Tsoka lake ndi lakuti sakakuyankhani, ali busy kuyankha mafunso ku Police kkkkkk!

RODGERS
RODGERS
3 years ago
Reply to  Wachiyao

Tonse Alliance promised us that they will end corruption that’s what they are doing taking to book all looters of our money ,that’s the starting point.

Boma
Boma
3 years ago
Reply to  RODGERS

Ndiye ma cadet a panga root office ya ndani?

Mj2
Mj2
3 years ago
Reply to  Wachiyao

Kkkkkkkkkkkkķ akomokatu ndimafunso ada agogo nyekhwe

Masilu ga liwata
3 years ago
Reply to  Dyera

inu mukufuna musamangidwe mukhale ndi misonkho ya a Malawi never sizitheka mumangidwe mubweze,ndipo zodikilira malonjezo ndi za ife inu mudzidikilira zanu zimene munavotera aliyense zakezake.

Nyomu
Nyomu
3 years ago
Reply to  Dyera

Kumangako ndizimene zidalonjezedwa kuti azasesa mbava zonse kuti dziko likhale clean. Ife tikusangalala nazo zimenezi

Medson
Medson
3 years ago
Reply to  Dyera

Koma chitukuko chomanga chokhacho akupanga
Koma sindinkumvapo ana aku university school fees ayisisa yiripabwanji
Good Tonse government
A malawi mnawanamiza

Malidadi
Malidadi
3 years ago
Reply to  Dyera

zoonadi

msundwe
msundwe
3 years ago
Reply to  Dyera

lonjezo loyamba ku Maula kuoite mbava zenizeni. Miseu pambuyo

Read previous post:
Malawi religious tension: Christians demand council pulls down offensive Muslim billboard

The Evangelical Association of Malawi have reacted angrily to a bill board mounted in Blantyre by Muslims which say since...

Close