Police arrest DPP security elite over reign of terror
Malawi Police in the southern region have arrested the notorious 14 members of the opposition Democratic Progressive Party (DPP) called Super 16 blamed for atrocities against the then opposition MCP and UTM.

Police spokesperson in the southern region Ramsy Mushani has confirmed the arrest of the 14 who were always armed and led a shadow paramilitary wing of the party during its reign.
“Our officers from Luchenza have indeed arrested them on crimes of assault, theft and malicious damage.
“They will appear in court after we sort them out according to their crimes,” said Mushani.
The suspected notorious DPP thugs are alleged to have torched the UTM vehicle in Mangochi and beat up severely rights activist Billy Mayaya in Blantyre.
No sympathy for DPP anthu oyipisitsa
China chake chichitika muno mu Malawi. Ili ndi dziko. Kamuzu Banda ankazunzanso anthu chonchi. What MCP is doing today is exactly what it did in 60s. It arrested all potential political leaders and technically killed all opposition parties such that by 1964, MCP was the only party left and they rulled with a heavy hand until 1994. Everybody lived in fear such that nobody could afford to voice out the ills of government. That scare tactic is the one which they want to use now. Inu simukudabwa kuti anthuwa akumangidwa pa tizifukwa tina tosamveka bwino? Let us remember that MCP… Read more »
There is nothing that will happen for as long as they are leaping what they had sown please dont think DPP ndi Boma No. DPP was a party that simply mistook itself as Malawi now they are harvesting what they had sown. We ae strongly behind the arrest to get the truth that has been hidden by DPP for long. Don’t worry you will have your day in court where evidence will be submitted, evaluated and verdict passed and
I agree entirely with you.
You are just showing yourself how dull and stupid you are.Who can support those naughty DPP Cadets the way they were doing?Its only you stupid fool.
What they (MCP, UTM and others in Tonse Aliiance) are doing is what we voted them for. Mumayesa dziko ndi lanu nokha. Ngati mumamva chizungu amati, “how clever or sophisticated you plan evil, somehow the truth will still come out” Those who wronged other must be punished.
Alangidwe amenewo,anthu oipa,zilombo,sizikuyenera kumakhala ndi anthu mmudzi,ali ndi zilope.nkhani ya kuvulanza/kupha sinkhani yabwino………………….iweyo ukuonetsa kuti mutu wako ndi wobalalika.usaiwale kuti anthu osalakwa ali mmanda ali mmanda pano.nawosotu moyo amaufuna ngati mmene ukupumila iweyomo.iwe wafa ngati.
withdraw your comment b4 COB to day
Mbuli zimenezo amazigwilitsa ntchito a DPP ZIMANGIDWE NDITHU, akaona ngat dpp sidzatuluka mboma Nyekhwe after Nyekhwe musanati mukadalira ma cadets
Nothing will happen chief. Pano it’s payback time and payback is a bitch. He who lives by the sword will die by the sword. This should be a person kwa aliyense. Osamayerekedwa ngati dziko lino ndi la munthu mmodzi kapena chipani chimodzi. For your own information, kumbali yomanga anthu this is just the beginning… watch this space.
What dpp planted it’s what they are leaping
This should be the example to tonse alliance
don’t feel you are at comfortable zone.
What is leaping pedegu iwe??
masiku forty akakwana akwana…….kulipidwa za misonkho chifukwa cho senza lupanga ndi phwitika!!!! oh my word !!!
teach them a lesson
burn them arrive , conquer them , plun them
Good job! Aone Nyekhwe amenewa! Anthu odzimva komanso a nkhanza!
Macadet mumayerekedwa mumaganiza dziko ndilanu
Nanga aja anatseka mseu ku Nsundwe ndi ku Mponelavbwanji salumangidwa?
Inu daily makomenti anu amakhala opanda nzeru kaya umbuli umakudzungudzani kaya.What crime did those commit?
MBULI NDIWEYO CADET
ndiwopusa ameneyu sanapite ku school cadet wachabechaeb
You are too brute to understand things. Don’t you know that blocking road is a crime?
Their were demonstrating and its hard to identify who did this.Moreover it was a peace demonstrations.
Cadet! Balirani chonchi.
killed the policeman innocently akayakha kwa Mulungu
He was killed on the line of duty.Besides,it was a mob justice.
Mmmmm man simukuzitsata. So pitanu ku police mukafunse kut mwawaangiranji ?
Inde. Nsundwe Barracks injatidwenso. Mukuwasiyiranji?
Hahaha!!!!! M’bale msundwe ndi victim wamva?
Katsekuleni mlandu nanu. Muona amangidwa.
Ahhhh komanso Boma la DPP ndiye kayatu. Bwanji silinawamange?
Anali a nyau nde mwini dambwe ali pa’ State house ka
TIKUDIKILA ZOMWE BOMA LA LERO LIMATINAMIZA PA CAMPAIGN TISAMANGAOMVA ZOMANGANA ZANUZO PANGANI ZOTI MUTHANDIZE A MALAWI. kUMANGANI KUTITHANDIZA CHANI IYAAA
Boma likuchita zomwe ife amene tinalivotera tinapangana nalo. Inu omwe munkasapota agogo aja, zanu zomwe mukufuna mukapemphe kwa agogo anu omwewo. Tsoka lake ndi lakuti sakakuyankhani, ali busy kuyankha mafunso ku Police kkkkkk!
Tonse Alliance promised us that they will end corruption that’s what they are doing taking to book all looters of our money ,that’s the starting point.
Ndiye ma cadet a panga root office ya ndani?
Kkkkkkkkkkkkķ akomokatu ndimafunso ada agogo nyekhwe
inu mukufuna musamangidwe mukhale ndi misonkho ya a Malawi never sizitheka mumangidwe mubweze,ndipo zodikilira malonjezo ndi za ife inu mudzidikilira zanu zimene munavotera aliyense zakezake.
Kumangako ndizimene zidalonjezedwa kuti azasesa mbava zonse kuti dziko likhale clean. Ife tikusangalala nazo zimenezi
Koma chitukuko chomanga chokhacho akupanga
Koma sindinkumvapo ana aku university school fees ayisisa yiripabwanji
Good Tonse government
A malawi mnawanamiza
zoonadi
lonjezo loyamba ku Maula kuoite mbava zenizeni. Miseu pambuyo