Sankhani Mkandawire makes u-turn, still with Bullets
Big Bullets defence pillar Sankhani Mkandawire has reversed his decision to quit the club and has returned to the champions.

Bullets general secretary, Harold Fote, confirmed that Mkandawire has returned to the People’s Team.
Sankhani announced he had resigned from Bullets but a delegation led by technical director Billy Tewesa convinced the player to change his mind.
“That is now a thing of the past. Sankhani is back with us after ironing out some issues,” he said.
Sankhani has been one of the shinning stars in Bullets and attracted attention of South African clubs. He was invited to Polokwane for trials with National First Division (NFD) side Black Leopards.
Three years ago, Mkandawire also had a stint with Carara Kicks in the South African NFD.
Follow and Subscribe Nyasa TV :
Agalu alomwe kwanu kukalima fodya kumpoto ndikukwera galimoto zathochi basi.
Welcome home sonny
Tsankhani Mukandawire ndiofunika inu a BB mudzamuchotse muli mudressroom. Asangakuchitiseni manyazi inu a Kondi choncho. Timanena paja kuti aTumbuka akuzikonda kwambiri. Chili chonse demo basi. Mwana anadyatu demo yake. Next time wosadzamunyengeleranso ayi.
Atumbuka mumatukwanisana nokha chifukwa chazopanga zanu mukalawa town BT/LL Cty
PA CHITUMBUKA BASI..iLI NDIE KHALIDWE LAWO KUZIKONDA..NO WONDER MAFUTA MWALE WA SILIVER AKUKANIZA MA PLAYER..NDIE CHITUMBUKACHO, MWANA WANE AKAONE KU MOZAMBIQUE
kodi kumpila atumbuka alikonso,mwayi ku netball, tabita chawinga ku women football sono first gentleman kumpoto first lady of leader of opposition kumpoto sono anthuwa tiwakwanitsa ? panopa i can believe that we cannot mutch these guys we are only pretending to be like them but we are very far to be inline with them. introduction of quota system is may be our tribes can get education but we are loosing the war of quota system. tiyeni abale tingogiva because sitiwakwanitsa anthuwa the more we try to oppress them the more they invent more ideas. I rest my case
the only reason w hate these notherners z bcz f our hostility t missionaries.
Atumbuka mukuwanyzawo ndiamene mukuwakakamilawonso: chiukepo,sankhani,chawanangwa…Pamnryelo pinu mose pamsundu pinu!!!
Sankhan, ndiwe player wabwino koma usayambe zozimva zikusokonekela. Think of komwe wachoka. The moment ungaiwale komwe wachoka chizakhala chiyambi chakugwa kwako. Osamapanga zinthu zot uzinyengeleledwa. B mature enough!
sankhani osamatilankhulitsa pambali usazabweleyzenzo uzaona
Goodlucky
Malawians we are one. Stop regionalism. Achewa ngati sitilimbikila pachili chonse achidwi adzitinjoya.
Matama basi umafuna kutchuka ndizopusazi.
guyz nkhani si yantumbuka mukulakwisa. Sankhani musamafulumire kusiya nsima mukuifuna zotipusisa ife sitifuna.
Guys,let us comment with maturity and responsibility… Poti wochokayo ndi Mkandawire basi atumbuka ati….He had his reason for leaving and its his decision to go back to Bullets….. Let us be constructive pilizi tisamanyozane.
Kodi. Atumbuka. Bwanjizonse kusogola
Sibweni wakupusikanga ndinjani kuti mupakana kughanaghana zakufuma ku timu iyo kulwande yakutukula ndipo waliyose wakumanyira.Heeeeeeeeeeeeeeeeee wanozga chomene kuwerera. Keep it up and nozgekanga za CAF sono vinyakhe ivi luwako.
I hope the officials will do the same with Kananji.Otherwise this is goodnews.
Please check these Tumbukasa critically in sports. It all started with Mwayi Kumwenda. Then her alongosi Tsankhani Mkandawire. Next time it will be the whole team since most players for every team are Tumbukas .Yet they say that they don’t enjoy the national cake of Malawi.Ufiti basi. Time has come for quota system in every discipline of sports for national teams. This is a wake-up call for national teams management. Don’t overload the team with only the MBwenumbwenus. Look the type of dribble these Tumbukas are giving to management of every team.Atumbuka sakuimvatu when it comes to fighting for their rights.Chindereismic concept.Take an example of Surestream in which you could hear names like Mkwate. In fact most players from Surestream mixed from north , central and south by looking at their names.
Amafuna abwelere kumkaya.
Good decision. A Sign of maturity. You’re a wonderful defender. BB motto!
Good news.
Chifukwa chake anamuchotsa u captain ndi chindele munthuyu
atumbuka afikapo kwao kuthengere
Atumbuka azikuzimvatu tsopano. Chonchi kuli konse ngakhale ku netball komwe. Awa ndiye alendo basi.
Inu a phodogoma zanu koma nsanje, ndi kudula anthu ziwalo
Akapezerapo wina udzalira ngati Kananji mphwanga amenewo akupusitsa. Tikachoka sitibwelera chifukwa podzakuchotsa adzakudzidzimutsa.