Joyce Banda attacks ‘deeply corrupt’ DPP govt: ‘I’m coming back to Malawi, come what may’
Immediate past president Joyce Banda, who is currently living in self-imposed exile abroad, has told supporters of her People’s Party (PP) that she will be back home this year but said Malawians need to be liberated from “deeply corrupt” Democratic Progressive Party (DPP) administration.

Banda addressed the PP supporters in an audio message which is going viral as people are sharing it through the WhatsApp.
In the recorded audio, Banda who lost the 2014 elections to incumbent President Peter Mutharika, accusesd her successor of treating corruption with kids gloves.
She lashed at the DPP administration for what she claimed was institutionalised corruption and assets stripping on State utility companies.
“I feel disheartened with the clueless government which is making our people suffer,” she said.
“Katangale ali ali tho tho tho!Kuba ku chipatala, kuba ku Tevet. Kuba ku Escom. Kuba ku water board. Anthu akusowa madzi, kusowa magetsi. Anthu akupezeka ndizindalama mmanyumba tho tho tho. Kuwotcha ma ofesi Makati. Koma lero Peoples Party ndiye chipani chimene achipezelera kuti adzichiseweretsa kumazunza atsogoleri ake.[ Corruption is deeply entreacnhed. They are stealing from hospitals, Tevet, Escom; They are stealing from water boards. People have no electricity, no water. People are being found with huge sums of money stashes in their homes (George Chaponda). Yet, at the end of the day, the People’s Pary and its leadership are the punch bags.]
Banda also said in the audio that she is heading back home “soon”.
“I am asking you fellow Malawians to pray hard, Satan has engulfed the country,” she said.
But Minister of Information and Communication Technology Nicholas Dausi hit back at Banda, saying she is making “unsubstantiated allegations, innuendos and political inertia.”
Dausi, who is also the official government spokesman, accused Banda of engaging on a crusade to tarnish the image of Malawi abroad.
Banda also said in the recording that the DPP won the 2014 elections on a stolen vote.
“What has happened in Lilongwe where the MP [Bently Namasasu of DPP] has been removed [by the court] is evidence the elections were rigged,” she said.
Banda said if ballots were examined in all constituencies and presidential race, it could have proved “how much the elections were rigged.”
She said: “This year will not end I will be back home. I am coming home come what may, even if they want to kill me but I am coming.”
Follow and Subscribe Nyasa TV :
palibe chosintha oloko mutabwera abiti hamala,inuo ndi a pitala ndiye bola tizuzike ndi pitala yemweyu.
bwera tikukufuna kuno wakuba iwe. usayese tizakumvera chisoni. unaba zochuluka sitizakusiya iwe ndi roy chule wakoyo.amati kachale kwanu konko.
kodi nanga nkhani ku CIKANGAWA yogulitsa mitengo/matabwa ku ZAMBIA NDI MMWENYE uja .anthu ambili anacotsedwa ncito opanda malipilo utalanda company from that fella mtse……lo uja??????????????????? ana aathu azimai kulephera sukulu. amai abambo kulephera kusamala mabanja ao coz of your greed. imeneyi unangoipsatila kaamba atidye nao anangoikhalila yet umati kukamba zolemba anthu nchito. mwana wako ndi iwe munazuza anthu, mwaocha eskom kuti zacamba unacita zijaso. kazibwera tili ndi umboni ose bwera uone.abale tigwilane manja apa. kodi aliyese angoti poti ndinali ku abroad nde ndikhale plesident! ZACAMBA. BWERA UONE UESA A MALAWI ALI MOMMUJA HULE IWE, SITEPE NGATI N’GONA
Iwe Abiti Ntila..nawenso wachonatu chifukwa cha cashgate. Kuba aMalawi anzanga. Yako ija yotakata…kkkkkkk
kodi azatani bakha uyu. ubwere ndi
-ndege yathu
-maina aamene anaombera mphwiyo paja ukawaziwa anyamata okamwera mowa ku Joni. ulendo ku ma Pub a Joni ndalama lolololo
-ndondomeko yomwe ukufuna azapange kuno koz u r just making noise. zumbwe
-kodi ana a MAKANYA unangonama cithandizo, sukuwathandiza coz of your greed. pakamwa ndi pa bomatu
> utazatofotkoza misonkho yathu komwe imapita
Matchona tatopa nawo
DR Moses Ku Central medical stores alipo mafia and giving contracts pa Buy Malawi Campaign to Malawi pharmacies opanda ODPP tendering, katundu is overbought and rotting in warehouses at Central medical stores,. Investigate Dr Moses ACB
Is Abiti Ntila on a self imposed exile or cashgate induced one? Kubha mayi uyu. Ufele konko wamva? Nthawi yako yotakata pa misonko yathu inapita. Go to hell and roast you mother and baroness of corruption.
Ndalama zakuthelani mukufuna muzabe zina pano mgodi ulimanja mwa anzanu kwanu kunatha mai
I have come to the conclusion that Dausi has only three or four verbs
Musatisokose Mai. Just come and retire quietly to Domasi, if you are tired of McDonalds.
A friendly word of advice: Should you still be serious about rescuing Malawi from the shackles of thievery and corruption, the best way would be to team up with Soldier Lucius Banda and move to MCP. PP is now in tatters which can never be patched up. You would never resuscitate the party in it’s present state and even the best of mechanics cannot rebuild the engine
And remember; Malawians are still in Cashgate shock which they suffered during your time. Your chances of escaping JAIL is if you were part of the new MCP government. On your own? You might as well speak nicely to Trump and stay in USA for good.
MCP &PP agree one thing tizawachose akubawa pampando atibera mokwanira, mama we miss alot of things we as a youths of this country tikuona kuchedwe 2019 kut tichose nkhalambazi,inu mayi mnasankha sosten be your running mate & CABINET YANU MAMA U HAD ALOT OF YOUNGERSTARS KMA LERO ETI CABINET YONSE NKHALAMBA SHAAAAAA SHAME TO PITALA.PIPO R WAITING KUT MZAWAPULUMTSE LIKE DAT TYM TIKUGONA KU FILLING STATION MAMA
PP bomaaaaaa 2019 mama i really miss u & YOUR GUD SKILLS OF LEADERSHIP not nkhumba ikulamulayi,anabera mavoti asakudziwa kut boma timayendetsa bwanji? He failed to running the minstry of education & justice ndie angayendetse dziko ? i hate kamagweru pitala.i wsh atangopanga resign yekha otherwise he wl die wth the anger of the malawians.iwe Dausi usiye kumnamiza pitala amwalira ngat bingu
Mwangokumana nonse mbava zokhazokha. Anawotcha escom si anali mwana wanu mayi….Paul Mphwiyo munamulembelanji ntchito yet you know ndi wakuba? Ndege yathu ili kuti? Munathawilanji nanga just after ma elections?
Nonse mukulowera m’boma kudzaba basi, musanamepo apa. Bwerani ndi ndege yathu yomwe.
I agree with dziwapo
Kapena mukubwera chifukwa cha nkhani ya visa ija? Mayi, inuyo panokha anakuberani mavoti angati kuti muzilephera mpaka pa no.3 chipani cholamura?
Wofooka mumayi iwe ..chifukw chake sitizakuvoteraso koma,zoona abandoning us
Munthu sumaononga kwanu kumathawlra kwa weni. bwelani tizaona kuti tipanga nanu bwanji
“liberate Malawi? From what? Kma abale muchita kulenga nkhani zoti axakuphereni? Wy kulengedza kuti mukubwera,mtima ifuna kuyambitsa phokoso mdziko lino basi.bwerani bwino bwino.okukondani akuondani,osatita chifukwa cholngolola ayi..osamayambitsa dala mapokoso.kumene mulikotu andale ake sakupanga mapokoso ngati amene mukufuna kupanga mukabwera kunowo…
DEAR MALAWIANS
IF WE REALLY CARE ABOUT OUR COUNTRY
TO MOVE FORWARARD
WE HAVE THE FOLLOWING PEOPLE FOR
PRESIDENCY COME 2019 AND BEYOND !!
NUMBER 1 MAJOR 1
2 USI
Lucius
The Rest at your own RISK
Bakha uyu ativutatu. Unayambira kuti ubwera muja bwanji sukubwera galu iwe?
Kwanu ndi kwanu. We are tired of hearing about you. When I see you I always think of throwing up. To he’ll you go
Mama we need you this dull professor is sleeping,the country is in a mess
We expect a gigantic alliance between Joice Banda and Lazarus Chakwera to remove this monster-DPP. CHAKWERA WORK HAD YOU ARE OUR HOPE
The Queen of Cash Gate is talking. It is the pot calling the kettle white!
Bin Laden style undressing people through tapes. we know you are coming not to challenge DPP and APM but because the no nonsense President Donald Trump has denied visas to all stupid and corrupt African politicians like you so that they go back to their countries face the tune of their corrupt actions. we are aware you US education visa expired with no option to renew. Your hide out is becoming smaller by the day. Next it will be Jacob Zuma to tell to pack since you have overstayed his welcome.
Abwana Dausi, inertia is a well known phenomenon in physics, as espoused in Newton’s Laws of Motion or Galilean Relativity. So, what is “political inertia”?
Regarding JB; well, Malawians have seen for themselves how utterly incompetent APM has been at his job. A former university professor who has proved to be so useless at running the affairs of the state. JB was a better leader than APM.
Look, at RBM there was Ligoya(Lomwe), then Chuka(Lomwe) and APM wants another Lomwe to take over? Tell me you are joking, or there is something seriously wrong with the president. A Chewa, a Tumbuka, Yao, Sena are not human beings? If he wants to be remembered long after he’s gone, advise him to change his approach!!!
Mai bwerani matchona akudziwa kwawo kwatha ndiye akungo dyelatu panopa ali pakala pakala
mpaka kuba ndindalama zaku chipatala zomwe zoti agulile mankhwala kkkkkkkkkkk.
Koma MATCHONA NDILIBE NAWO MAU
Mubwele muzafikire kumudzi. Osati muzizatisokosera ife. Tinatopa nanu amayi nthawi yomwe munagwera boma. The country had no direction. Muli ndi ukadaulo wina osati kulamula dziko. Palibe angakupheni mayi.
The one who sold us is Bakili.
100% correct
To say the truth kubwera kwa JB Ena adzamva mpedzedze. Iwe amene ulibe udindo Ku chipani cholamula sukudziwa tension imene ma bwana ako alinayo. Mayi ameneyo ndi big threat Ku Malawi akusasulani koooopsya.
plz mama JB come back to your mother land in the same way you left it.you are not Dr H Banda whose coming back toMalawi made part of our history books for this generation and generations to come for it marked liberation from samundas.in your case,you are a smugglar.you deal in own income generation activities which you told us that you learnt kutakata at a tender age and nothin to offer to malawi fox.after all malawi fox did not vote you into the presidency.if anythin you should be the last to coment on corruption.Lutepo,bwana Kasambala and,,,,,, Have No Kind Words With You.Just Come Back And Face The Music Kkkkkkkkkkkkk!! Kaya!
What comes shall be, please come
mukamabwera mutibweretsere ndege yathu, plz.
ndalama za oil zaku Nigeria, zinazo tidzakuuzirani konkuno
mukabwera
Dirty politics!
Come, our jail is awating you. The only thieving accidental president Malawi has ever produced.
Narutah
We know last time Dpp tried to kill her. Try again and wina adzapitanso.
“Home is home though it may never be so homely.” I rest my case.
Mchona tatopanaye
Mchona came with only a suitcase. But he is very rich. A Malawi why are we letting him steal our resources. ?
This come to Malawi with only a Suitcase and mukati Mwa munalibe kanthu suwa.
Ta top to be ruled by ?Mchona who an American citizen
Mama should tell the world that she is going back home just like Kamuzu and Chihana did.
Rubbish woman.
If you were able to kill poly student and Njaunju and some who had created accidents then we also know that you try all your dirty tricks including poisoning
Her .
Mai when you let the whole World know. Address Your supporter at kia airport.
Bring also reporters from abroad to cover your arrival. We wish you all the best
To liberate us.
Koma Mai we need you in Malawi. If they dare kill you then this country
Will be ungovernable as we will fight back with force. Don’t think Malawians
Are stupit . This time it would be Tit for Tat
Joyce, just come back. It wont help us to hear your tantrums while abroad. How many times have I heard you say you are coming? I just want to see you back here no phokoso. By the way, do you have anything to offer Malawians? Time will tell
Bwerani Amayi. Takusowani. Enawa atikwana.
Come back Mama we miss you. Anthu awa atitopesa ndi nkhanza zawo
Amakubera ma vote iwe uli kuti. Chinakuthawitsa ndi chiani kumalawi kuno. Mmene unayambira kunena kuti ubwera. Bwera ugwidwe uone
please just come madam former President
Amai inunso nzeru nzochepadi kwabasi. Munthu kumudzi kwanu kuchita kulengeza kuti ndikubwera. ingonyamukani muzibwera. Chipani chanu achipezelera chifukwa chiribe mtsogoleri. If you’re patriotic just come and start waging war against DPP. Osaopa sangakupheni.
koma ziliko, tabwerani tione
JB as fondly called by her deluded followers is an incompetent person to comment on issues affecting this country. Malawi is in no way missing her and we are at a better place now than when she left the Presidency and the country. Being silent is the best thing she can do for Malawians.
amayi mutu wawo sukugwila bho bho abalalika kkkkkk akusowa pofela awa aaaa akhala moyenda long tym nde asowa ntengo ogwila he heee atipeza pa nyasaland kkkkk amaona ngati athawa kkk hom is best athela manjatu awa.
Welcome madam we are keenly waiting for your arrival we miss you alot. Kuno zinthu ndiye zavuta zedi.
come mama to redeem the country from thieves
Just come back silently MAMA. We have heard about your coming back several times but you didn’t.
NO-ONE will kill you!! WHY and for WHAT?
Munthu akamafa amagontha makutu ingofera komweko. Sibwino kuti uzaononge mbiri ya APM kuno.pitiliza kumwa magazi ndi Bushiri wakoyo.