Ligomeka calls it quit as Bullets treasurer
Journalist Brian Ligomeka has confirmed his departure as Big Bullets FC treasurer.

Ligomeka said he has resigned in protest against main supporters committee’s recent call for the resignation of the entire executive board.
In a letter dated April 6 2015 addressed to the club’s acting chairperson [Sadik Malinga] and the entire executive board, Ligomeka states: “Following the call by the supporters committee that the members of the executive committee should resign—which in my view violated the club’s constitution—coupled with recent developments in Bullets FC, I hereby tender in my resignation from all the positions.
“In case of any query on any transactions I handled in the club, I am available to offer explanations. From today onwards, I will be an ordinary supporter of the team.”
Kkkkkk ukoooo!
no mata wat our haters wanna be saying but we won’t giv up coz BB tachoka nayo kutali.
Mavuto onsewa ndi chifukwa cha namachende otchedwa Kondi Msungama,munthu osaphunzira komanso osamva ,mbava mbambande pa Malawi.Fischer Kondowe ananena zoona kuti ma players ndi makasu a Kondi,Mbebuwa ndi Ligomeka.
We comment on the issue at hand enanu mutipeze mkalasi tikuphunzitseni how to comment
Tiziona
I hear Nakoma has writen Fam & Sulom re-calling back Tizgobere Kumwenda & Victor Limbani coz BB has failed to pay transfer fees, with all these debts & wrangles will BB manage to buy these players?
Yako ija
Neba uli pa ululu owopsa,,,,,,ukhala opanda atsogoleri
I can forsee BB grabbing all cups and legea title this season again, no matter what. Ubwino wake akuchoka ndi ma official not players. Victor Limbani has denied the allegation of going to Silver and instead Nakoma is about to take BB to court if FAM fails to settle the matters: in what manner I don’t know.
god be with us, l know bullets very well…..
Koma ndew eeee kwaipa kumeneko kkkkkkkkkkkk, kaya zanu ndi bubu yanuyo , simunati!
malawi has benefited in bullets’s playing in CAF….even if it was nyerere or any other team….we would carrt the flag of MALAWI…so be sportsmen….
Comment
BB, what a business model! you embark on a multimillion venture on nothing?! When BB were joining the CAF competition, they were already indebted, failing even to honour the players’ dues. This daring is senseless. Now we are saying supporters are going to run the show with negative 30 million kwacha!? Supporters, not those chamber smokers, should meet immediately and strategize on how to woo the Corporate world to pump money into the club for its survival, otherwise this team is finished.
Paja akupitilira nu caf eti?
Comment Its apublic team so there are many who can take that position but if you are atrue BB supoter you shld encourage her/him.Big Bullets,team 4 the pipo simada nkhawa ndi zolankhula za akapolo ena osakonda mpira
Club iyi idzakhala yopanda executive 1time
walter ananena kuti simukwanitsaaa! he’s a graduate from chanco and a manager at a multinational company so he knows things. inu mitu bii mwati mulowa CAF. musova
Ndaxiya kusapota bb nane
Wachita Bwino Nzanga Zikwanje Sisanafike Kwa Iwe.Ukanakhala Wina Ukanasia Kusapota Bb,bwera Ku Nyerere Akukhapako Kumeneko.
Comment Inde Zikanyanya Kumazitula Kuti Ena Azione. Mwachita Bwino Mupume
Musova simunati paja pali over 30.0 million ngongole. 15.0million ngongole ya Ma SMS ku TNM,eiiish Akatapila asanapasidweee,Kusamva tell mee??wat is the Benefit u hav got playing in Caf ??apart from the Misery that u hav created??
Nkhosa zopanda m’busa ndi chonchi basi”, eish bb
The stupid supporters n trustees should take over
NG’OMA YOLIIRITSA SIYICHEDWA KUPHULIKA! BB MADE ALOT OF NOISE, NOW ITS UR DOWN FALL!
Salimba a BB ,
Koma abale ndichani kodi
Team ngati ya kung’ombe…..asiyileni masapota
Aaaa palibe chilungamo apa
Mmmmmmm! Zavuta ku team yanga
downfall of the country’s soccer power house.
Relagation to the second tier league, popularly known as the Premier, is imminent next season!
Nanga titani ,as they journey now becomes tough for reds
enanso amene atsala achite resign
BB ikuonongeka chifukwa cha mbava zimenezi. Zichoke zonse basi.
Mukufuna mupeze ponamizila mukamaluza,mbuzi inu bb!bb chani apa.BULLETS timu ya mbuli,masavege,mbava,zisiru,makape ndi asizina nditole.WAWA BFMW FC known as NYELERE ZA MANOMA
Koma Neba.Kunjaku akuti abweze 30 million yangongole treasure nkumachoka.Onena adanena kuti CAF musalowe mulibe ndalama koma Neba liuma
Chinambalala ku BB
Zovetsa chisoni ndale mumpila kugwetsana tiona ngati ma player zawo azilandila munthawi yake,
Too much savagery at the club being perpetuated by greedy and small brains of supporters with the blessing of some misguided trustees who thinkknows they are owners of the club. Am a life long big bullets supporter too but the current pathetic state of affairs will only take back the clua into decline. These small minds in fat bodies should know they do not own the club and they do not run the club. You too trustees, rise to the occassion and uphold the teams constitution if you are indeed trustees who understand your fiduciary duties as trustees and bring this mess to an end.
to hell you guys
BB YATHA kikikiki
Nanga akuti ayenera kumulipira player aliyense medical scheme ku masm. Azitha?
Akutinso alembe chani chani kaya, azitha?
BB SISEWERA NAWO LEAGUE, YATHA kikikiki
BB ndiye yolimbayo. Gwa! Ngati naphini.
Ziwoneka
That is the only way to go my Brother be4 ”Operation Cane Knives / (Dzikwanje).
the seeds that kondie sow have started flowering, i dont know what type of fruits they will bear. Ife mabanker ndife okwiya timafuna idzikuchinyani muli nonse mutakapanga training ku khartoum and comoros
Timanenatu Ife Kuthako Kwa B B Uku
BB ikutha ngati makatani!
Bad news.
KOMA ZILIKO
Mwoana kuti kulibe chomwe mutabe mmene zasokonekeramu mwathawa nonse, machende anu!
kupanga zinthu mwa umbuli zotsatira zake ndi zimenezi atsala ma player onse athawako ndithu.
Koma ndiye zavutiratu ku BB. Koma mulimba?