Parliament approves 2 DPP officials to take up diplomatic positions: Khwauli, Chazama
Parliament’s Public Appointments Committee has approved President Peter Mutharika’s appointments of two Democratic Progressive Party (DPP) officials to take up diplomatic positions in Malawi foreign missions.
The committee has on Thursday approved the DPP director of political affairs Khwauli Msiska to be the High Commissioner to South Africa.
He was approved by the committee with 17 votes out of 20.
Director of women in the DPP Cecelia Chazama is now Malawi’s ambassador to Ethiopia and the African Union.
She won the committee vote by 17 votes to five.
She replaces Chimango Chirwa who has been recalled.
Follow and Subscribe Nyasa TV :
Iwetu ngati ukulankhula motumbwa chonchi poti uli pa joloza kuola manyi aagalu ulinitsoka ngati ndiwe mmalawi udzimvere chisoni ndi mtundu wakwanu unless ngati ndiwe mlomwe ogulisa second hand car or njinga zakabaza ya ndakumvetsa. Koma ngati ndiwe mmalawi kuwawa kumene atamve a mcp utm iwenso chimodzimodzi suudya dpp kupusa. Wamumva madalaako akuti akupanga condemn mpinganjila wa dpp yemwe amafuna kupanga bribe ma judge pali nzeru apa. Amene akupita kunjawo congratulations ndi nthawiyao iwe even cent yao sudzainunkhisa.
I can imagine why khwauli is silent
Most leaders in blue party have no vision for the country. Amalawi tili pamoto,eish. Without using merit it will be difficult for the country to develop.The country is moving so many steps backwards instead of moving forward with better developments to reduce poverty amongst Malawians.
A kongelesi ndi a Yutemu mukumva kuwawa? Ndiye simunati, inu mukadakhalabe ku opposition mpaka 2084. Kuwina zisankho ku Malawi kuno amatha ndi a DPP, kuluza zisankho amatha ndi a Kongelesi, ikakhaka Yutemu ndiye olo chisankho cha 2024 kuzakhala kulibe.
Wishing all the opposition kuluzanso kopambana in the pending court ruling on the shameful election petitions
Ukunamatu iweyo…DPP’S time is OVER! mukhala mukulira chaka chake ndi chino !anthu odziwa kuba,kupha ndi kuononga
People who will add zero value. God help this frustrating country and give us a new leader.
Nsanje malume izakuphani!
Khwauli uja ankafuna third term eiiish
kkkkkkkkkkkkkkkkkkkk kwasuzga
Ndiye mukumalephera kukopa anthu odzachita malonda (ivestors ) ku Malawi, kumadikira President akugwirireni ntchito ngati mumamugawira malipiro anuwo. For sake. Thom Mpinganjira ndiye koma tikum’manga abwerera ku jele, kenako timanga Brown Mpinganjira mwini film.
The timing of these appointments is rather tricky. In the LIKELY event of change of government in the coming months, these diplomats will be recalled.
Chiwoneni chi Khwauli kumaso ngati njati….kukonda ndalama more than abale ake……mxiii