ACB investigation officer Kondwani Zulu fired
Anti- Corruption Bureau (ACB) investigation officer Kondwani Zulu has been fired overmisconduct, Nyasa Times understands.
A source, speaking on condition of anonymity, at the graft-busting agency’s headquarters in Lilongwe said Zulu has been fired over “misconduct.”
Investigative Unit of the bureau has been faced with concerns of leakage of documents.
More to follow…
Ungenjerwanga yayi mzara wachindere ni awo wakuleka kutemwa chalo chawo. If ACB was really for anti corruption sakanakuchotsa ntchito
Mukazunza anthu ena osalakwa expect inunso kuzunzidwa musanalakwe one day. Mulungu anakupatsani ntchito yabwino koma ena monga anzathu ku ACB, POLICE, a ma khothi ndi ena timayesa mwayi ozunzira anthu ena kuti tidziwike kuti timatha ntchito. Ayi, Mulungu sakondwera ndizotere ndipo amakulandani ntchitoyo nkupatsa ena oyisowa. Mabanja anu azazunzika, ana anu azalephera kupita kusukulu, abale anu azasowa chithandizo chanu ndipo inu nomwe muzasowa mtendere. Tiyeni tigwire ntchito yathu mokomera Mulungu nthawi zonse.
Akulu osamagwiritsa ntchito dzina la Mulungu posapota zoipa. Kupanda report ya ACB ija kuwululika bwenzi titaziwa kuti Mutharika ali corrupt? Ambirife timathokoza kuti chifukwa cha chisomo cha Mulungu, the report was leaked.
ili ndi ziko lawo la amalawi chifukwa chani mumuzuze muntu chonchi ndi nkani zopusa ngati zimenezi , the all government kumachosa kumalimbana ndi mwana ngati ameneyi, may 2019 is coming amene mukuziona ngati madolo muziwaso sipano mukuchosa anzanu
Has he been fired or his contract expired and has not been renewed?
Kafuneni ntchito kwina or start your own private investigations firm ku ACB nkwachabechabe!
Stupid Zulu,now look,primaries for UTM are still on go to your master.Look at your wife and kids now,big as you are getting involved in pleasing a political loser.ALAS Watch your buttock
@ tman
Abale dekhani Musathe mau. Mudane naye chifukwa choti mukumuganizira kuti anapanga leak report yoti a president anu amalandira Ma kickbacks (mk145 million , 5 vehicles). Dziko lonse likudziwa kuti a president anu a Mutharika ali ndi mulandu. It’s just a matter of time azayankha. Nyansi zipose kukhala ndi president wolandira Ma kickbacks. Shame on you and your kickbacks receiving president. At 80 yrs busy stealing for what ?. Shame
The idiot was selling information to suspects , unprofessional arse wipe ..He should have been fired long time ago ,happy new year asshole
Koma ndiye ungatukwane m’Chingerezitu! Kutanthauzira kwake m’Chichewa ndicha? Kkkkkkk!
@ Arafat
Better sell information than steal poor people’s taxes . Look at that poverty stricken woman and man in the village heavily burdened with taxes which your president is busy chewing in form of kickbacks from inflated government contracts. Shameful and disgusting. You should be worried now because this guy has too much information akumalidzani ndithu.
@ Arafat and tman
Sorry I choose to differ. If your accusations and allegations are true then this Zulu guy is a national hero. Courtesy of him we atleast now know that a president athuwa ndi munthu otolatola. Kapena Chichewa chomveka bwino as a nation we now know that tili ndi president wa Ma deal. Uyutu kaya mumutani kaya koma akupwetekani uyu. Tsoka mutharika ndi ndi DPP poti Zulu watsikira konko
@ Chaka
Well said buddy . We have vultures trading as our leaders. Shame indeed on him. At 80 kumapanga ma deal. Sickness of highest order.
Mumulipila. Give him back his job
TELL US YOUR SIDE OF STORY
BWANA ZULU !!
Arrest for leaking 145 million? if it was not leaked it was expected that ACB to write that Karim and CO are cleared of any wrongdoing!
This guy (Zulu) is a political material to other parties because it seems he has credible information. Watch his tongue