Malawi Police, officers face each other in Court over promotions
The High Court in Lilongwe has set October 17 as the day Malawi Police Service management and 53 of its officers are to meet for mediation over promotions.
Supreme Court and High Court registrar Agnes Patemba has confirmed that the case of the 53 serving police officers who are demanding promotions will now go for a court sanctioned mediation process.
The 53 officers took their employer, the Malawi Police Service to court after they were allegedly sidelined during a promotion galore after restructuring process.
Lawyer for the disgruntled police officers, Gift Nankhuni, said the future of the case will depend on the outcome of the mediation process, saying the case can either be settled out of court or it might go in court for full hearing.
pitala bodza. amangoti akalezebwa mmawa kukaca ndi matsile kumangobwebweta.
ndikukwezhyani pa ncito. ndi izi lelo. mmanamizika kukamwa tea kusanjika nkumukodza musanafike kunyumba.
audience audience audience mupwetekekela zomwezo
kkkkkkk koma ma cadet awa
Cadet ndi cadet kubelana. Zimbava zokhazokha
2 much dyela ndi bodza from your pumbwa
Chimwapasa Chikadeti.
ZA MA CADET OKHA OKHA IZI !!!
ZITAYENI
Better should go for hearing
Eish a Gift Nankhuni zimenezi ndizo zanu osati ndale athandizeni odandandaulawo ma promotion anji omaona kochokera osati maphunziro