Police arrest protester with lethal weapons for HRDC demos
January 16, 2020
Owen Khamula -Nyasa Times 53 Comments
Malawi Police in Lilongwe have arrested a protester with lethal weapons he was found with in cartons on his way to the Human Rights Defenders Coalition (HRDC) sanctioned protests.
Richard Moyo who was found with 25 catapults
Police say they are keeping in custody 43-year-old Richard Moyo who was found with 25 catapults, 17 stones and machaka, 11 knives among others.
The law enforcers say they pitched an adhoc road block at Njewa where they searched each and every passenger of vehicles and Moyo had these weapons in a minibus from Mpingu.
Armed Malawi Defense Force and Malawi Police Service have also a joint operation road block mounted at Kapani – Roberts at Kanengo, in Lilongwe.
Both the army and police officers are searching both public and private vehicles entering into the city.
Apart from the thorough search of vehicles they are also searching people travelling with hand luggage.
53 replies on “Police arrest protester with lethal weapons for HRDC demos”
Lengeni kugulitsa ndi manati ndi miyala.
.Zimachitika kuti izi?
LETHAL???!!! If these are lethal then mfuti ndi Weapon of Mass destruction…..WMD Kukakamula!!!
Komatu kunena zoona munthuyu mmene akuonekeramu nanunso apolisi mudzikhala ndi manyazi. Malegeni awiri mkhosi ngati zilidi zida zoopsya mutumizeni ku karonga akateteze nyanja kwa ma taifa a nundwe athandize ntchito ikukukanikaniyi
Umatitu uchenjere lero ndi zimenezi,,pamenepo kuzuzisa mkaz ndi ana nkhn yake ya ziii…
Amupanga bwino
The man might have been on his way to selling these ma legeni. When did these become LETHAL WEAPONS? or do you even know what a lethal weapon is? Sad that Malawi has these MBUZI as law enforcers. It’s about time the country started recruiting educated police officers.
Goliath was killed by David who threw a stone onto his forehead!
Iwe mbuzi ndthu
Surely mtundu oti umaenda ndi zikwanje, zibonga ndi nkhwangwa nkumatema anthu olephera kuyankha ma sign language awo will not find it odd and suspicious for a man to carry catapults with its stones in an HRDC demo bound lorry!
By the way didn’t you hear during last week
HRDC demos kuti security officers were attacked and seriously injured by the same catapults?
Ine I am now 100% sure that HRDC, MCP and UTM just want to bring chaos in Malawi and sadly they are enjoying state protection. With the already high political tension and fast approaching D-Day (judgement day) the last thing the security forces should entertain is somebody or organisations to fan the already high tension. Khondotu imayamba poyerayera aMalawi
Amapita kukagulitsa kutawuni…..ndiye anagokwera nawo galimoto ya a mademo…….ndiyogwira kwambiritu mukhoti!!
Achewa ambiri ngozelezeka, chongonva kuti kuli ma demo iwo akuona ngati ulenje. Ma demo si ulenje achewa woti mpaka munyamule carton ya machaka ndi malegeni. Kunvetsa chisoni, ulendo okapeleka kalata kwa director of ACB, legeni yachani?
A Chewa,
Zikufikitsani pati izi? Mukupepelatu mmalo moti mulimbikile kulima fodya. Ndipo ndikukaika kuti kodi ogula fodyawo abwera chaka chino ndi zipolowe mukuchita inuzi?
Malegeni sitigulitsa ndi miyala yomwe, tamuoneni munthu kunzunzikira nkhani za weni, ndi ufa omwe kunyumba alibenso. mmalo momakapalira chimanga kumunda kulimbana ndi ma demon, next year muzizati njala boma lalephera, pali nzeru?????
Police’s definition of “Lethal Weapons” is too childish and laughable. Was Moyo going to distribute them to protestors?
Release the man for heaven’s sake.
This is Malawi police cadet and Dpp propangand just try to damange the image of demos.
our constition does not allow people to demonstrate while armed. The nsundwe lorries are always full of stones hence ochewa should face the law. If we tolerate carrying stones one day will work to find people carrying grenades.
He looking like not worried at all pa easy . So ma box a miyalayo muli golide kapena diamond kkķkk koma apolisi amadelela amphawife bwanji shaah amifuti kuwataya. Kodi msundwe rapist ili ndende yakuti .
Vigawenga vimangidwe basi
When did a catapult become a lethal weapon?
And knife has now become what in Malawi, a weapon of mass destruction I guess…….kkkkkkk
Iwe nchewa wopusa kwabasi. Don’t you know that late Supt Usumani Imedi was attacked by these same nyau fools using the same catapult before they descended on him and exerted the fatal mob justice? Sunamvepo that s person has been killed using a knife? And with your idiotic brain think this is a laughing matter? Fool. Mwayaluka lero.
Idiot He had metal nuts as weapons..That can blow your nose. Aftreall he has confessed that he was sent by a bouncer known as Loka to distribute to demonstrators..
You can go and ask Superintendent Usumani Imedi, he will give you answers whether stones and catapults in the hands of angry savages can kill a person or not.
Send him to karonga to protect the lake if they are really lethal weapons.
🤣🤣🤣🤣🤣🤣 Lethal weapons Malegeni ogulitsa?????
Sunawerenge mu Bible kuti sitifano anaphedwa ndi miyala by anthu ankhwidzi ngati inu achewanu?
This man cannot bribe judges.
Poor fellow just innocently selling legeni for hunting birds. There are no jobs in this useless economy.
nde legeni atatulutsa ndi miyala yomwo . Get real. These are the bastard that stole chickens at CP feeds
Tikamagula legeni timayese ngati anakozera mphira yotanuka bwino ndiye wogulitsa amafunika azikhala ndi minyara kapena machaka yoyesera mchifukwa munthuyu anali ndi zosezo. Amagwira olakwika mdalayu ndi vendor.
Matchaka regeiu galimotoya a demooo
What abt stones, they were for sale too
This is stupidity of the highest order for those who have arrested this guy…. Inu simunawone anthu akugulitsa ma legen .. Mu town .. Mxiiiiiii…. Msiyeni…. azipita kwa would
Legeni umagulisa ndi ma but…ndi miyala take..
Go and bail him out you fool…mxiiiii!
Arrest those who wanted to bribe the judges Please !!
What ever you can not conclude. Have you stopped people from doing business in the items? How do you conclude then?
He had the items so what? Has he told you the reason for carrying such? How then do you start speculating?
Why were the military personnel carrying guns? To kill and if yes why not arrest them
Nyasa times are you sure he is not a Cadet diverting the country attention?
DPP can apply all the known tricks but they cannot stop the nation’s destiny….it is long overdue!!
This guy sells malegeni ku ma security companies for the guards to use during night patrols. Amzake amayima nawo along Kamuzu central hospital – Nature sanctuary road. Propaganda basi!
Aakeera galimoto yopita ku ma deomostratione serious
You do not conceal items for sale you stupid fuck! Plus legeni sagulitsa ndi ma nut and miyala yomwe. Anthu openga mukuganiza bwanji? Admit that ku ma demo ena you have your own agenda.
I really believe the poor guy was eying a lucrative business of selling these deadly weapons at the demos, rather than using them himself. Either way he’s probably the most stupid of the demonstrators.
Is this a serious security issue? I have seen a lot of people carrying and selling catapults in town, how many were arrested? Is it a coincidence that we had HRDC led-demonstrations that’s why the poor man is arrested?
What about those who try to bribe our judges at the ConCourt, are they going to be arrested kapena ayi?
This is putting things upside down. Leave the poor man so that he sells all catapults PLUS stones. He only wants to feed his family, period.
Ife amene takulira kumudzi, legeni imayenda miyala limodzi for it to be usable. Palibe nkhani apa. Leave him. M’malo mogwira milamba ndi nsomba zikulu-zikulu, mukugwira matemba okha-okha bwanji?
Masiku ano, catapults are used by security guards and other security personnel but in the village, people use it for killing birds, snakes, etc.
This is an obvious propaganda, amutuma anthu wosafunila dziko zabwino kuti atenga zida kenaka amugwire aziti ndi wa HRDC wofuna zaupandu…….palibeeeeeee…………..more fire HRDC! Malawi asinthe basi……….
Vuto la anthu a nyau simufuna kuvomereza mukalakwitsa!
Agwidwawo amangidwe basi ndi awo omwe amenewo ife tayenda bwino popita ku ma demo sitikwera minibus. Timayenda zamadulira
lethal weapon is the dicks of those police officers shamelessly raping girls in uniform like its war torn DRC! And still walking scot free and having the audacity to quickly arrest Jessie and Timonty and friends over the girlfriend termirk story but not these officers that raped and abused people in Nsundwe. Selective justice cover up…..all must face the law equally and been given a chance to appear before the court for self defence.
What of your own dick idiot? Legeni is the symbol of your foolish boss Zeze Arafat. Mwagwa nayo lero abakha inu.
You are just one pathetic idiot who cannot face reality as it is. So to you it was better for this beast to vandalise property and kill innocent souls in the name of “peaceful demonstrations”. You truly know that the Nsundwe rape issue is just a cooked up story by HRDC and some wasted brains like yourself. With this greed you will allow thieves to rule this country forever. We surely need change but with this approach of yours, I would rather go for the devil I know. Wise up people and be the true change we are looking for, not this savagery
Nanaga poti mipeni ndi malegeniwo amapita nawo kogulitsa, mwa nthawi zonse. Mutayeni ndi business yake iyi. Kagwileni wochita bribe ma judge osati wpnyamula malegeni.
Zopusa!
What did the idiot confess? Amagulitsa ma legen ndi machaka ndi miyala ndi ma nut omwe? Ask Arafat Hamdan the Boko Haram leader like this ugly Mtambo
Like thieves ruling now.
@Patrot, you are a die hard cadet. everyone here knows about that. Unasowatu pakatipa pa forum pano. Welcome back.
No insults please good Malawians ngakhale muli okwiya osatukwanana
Lengeni kugulitsa ndi manati ndi miyala.
.Zimachitika kuti izi?
LETHAL???!!! If these are lethal then mfuti ndi Weapon of Mass destruction…..WMD Kukakamula!!!
Komatu kunena zoona munthuyu mmene akuonekeramu nanunso apolisi mudzikhala ndi manyazi. Malegeni awiri mkhosi ngati zilidi zida zoopsya mutumizeni ku karonga akateteze nyanja kwa ma taifa a nundwe athandize ntchito ikukukanikaniyi
Umatitu uchenjere lero ndi zimenezi,,pamenepo kuzuzisa mkaz ndi ana nkhn yake ya ziii…
Amupanga bwino
The man might have been on his way to selling these ma legeni. When did these become LETHAL WEAPONS? or do you even know what a lethal weapon is? Sad that Malawi has these MBUZI as law enforcers. It’s about time the country started recruiting educated police officers.
Goliath was killed by David who threw a stone onto his forehead!
Iwe mbuzi ndthu
Surely mtundu oti umaenda ndi zikwanje, zibonga ndi nkhwangwa nkumatema anthu olephera kuyankha ma sign language awo will not find it odd and suspicious for a man to carry catapults with its stones in an HRDC demo bound lorry!
By the way didn’t you hear during last week
HRDC demos kuti security officers were attacked and seriously injured by the same catapults?
Ine I am now 100% sure that HRDC, MCP and UTM just want to bring chaos in Malawi and sadly they are enjoying state protection. With the already high political tension and fast approaching D-Day (judgement day) the last thing the security forces should entertain is somebody or organisations to fan the already high tension. Khondotu imayamba poyerayera aMalawi
Amapita kukagulitsa kutawuni…..ndiye anagokwera nawo galimoto ya a mademo…….ndiyogwira kwambiritu mukhoti!!
Tinawonera Goodall akuwombola gogo mnzake Chapondatu!!!
Achewa ambiri ngozelezeka, chongonva kuti kuli ma demo iwo akuona ngati ulenje. Ma demo si ulenje achewa woti mpaka munyamule carton ya machaka ndi malegeni. Kunvetsa chisoni, ulendo okapeleka kalata kwa director of ACB, legeni yachani?
A Chewa,
Zikufikitsani pati izi? Mukupepelatu mmalo moti mulimbikile kulima fodya. Ndipo ndikukaika kuti kodi ogula fodyawo abwera chaka chino ndi zipolowe mukuchita inuzi?
Malegeni sitigulitsa ndi miyala yomwe, tamuoneni munthu kunzunzikira nkhani za weni, ndi ufa omwe kunyumba alibenso. mmalo momakapalira chimanga kumunda kulimbana ndi ma demon, next year muzizati njala boma lalephera, pali nzeru?????
Police’s definition of “Lethal Weapons” is too childish and laughable. Was Moyo going to distribute them to protestors?
Release the man for heaven’s sake.
This is Malawi police cadet and Dpp propangand just try to damange the image of demos.
our constition does not allow people to demonstrate while armed. The nsundwe lorries are always full of stones hence ochewa should face the law. If we tolerate carrying stones one day will work to find people carrying grenades.
He looking like not worried at all pa easy . So ma box a miyalayo muli golide kapena diamond kkķkk koma apolisi amadelela amphawife bwanji shaah amifuti kuwataya. Kodi msundwe rapist ili ndende yakuti .
Vigawenga vimangidwe basi
When did a catapult become a lethal weapon?
And knife has now become what in Malawi, a weapon of mass destruction I guess…….kkkkkkk
Iwe nchewa wopusa kwabasi. Don’t you know that late Supt Usumani Imedi was attacked by these same nyau fools using the same catapult before they descended on him and exerted the fatal mob justice? Sunamvepo that s person has been killed using a knife? And with your idiotic brain think this is a laughing matter? Fool. Mwayaluka lero.
Idiot He had metal nuts as weapons..That can blow your nose. Aftreall he has confessed that he was sent by a bouncer known as Loka to distribute to demonstrators..
You can go and ask Superintendent Usumani Imedi, he will give you answers whether stones and catapults in the hands of angry savages can kill a person or not.
Send him to karonga to protect the lake if they are really lethal weapons.
🤣🤣🤣🤣🤣🤣 Lethal weapons Malegeni ogulitsa?????
Sunawerenge mu Bible kuti sitifano anaphedwa ndi miyala by anthu ankhwidzi ngati inu achewanu?
This man cannot bribe judges.
Poor fellow just innocently selling legeni for hunting birds. There are no jobs in this useless economy.
nde legeni atatulutsa ndi miyala yomwo . Get real. These are the bastard that stole chickens at CP feeds
Tikamagula legeni timayese ngati anakozera mphira yotanuka bwino ndiye wogulitsa amafunika azikhala ndi minyara kapena machaka yoyesera mchifukwa munthuyu anali ndi zosezo. Amagwira olakwika mdalayu ndi vendor.
Matchaka regeiu galimotoya a demooo
What abt stones, they were for sale too
This is stupidity of the highest order for those who have arrested this guy…. Inu simunawone anthu akugulitsa ma legen .. Mu town .. Mxiiiiiii…. Msiyeni…. azipita kwa would
Legeni umagulisa ndi ma but…ndi miyala take..
Go and bail him out you fool…mxiiiii!
Arrest those who wanted to bribe the judges Please !!
What ever you can not conclude. Have you stopped people from doing business in the items? How do you conclude then?
He had the items so what? Has he told you the reason for carrying such? How then do you start speculating?
Why were the military personnel carrying guns? To kill and if yes why not arrest them
Nyasa times are you sure he is not a Cadet diverting the country attention?
DPP can apply all the known tricks but they cannot stop the nation’s destiny….it is long overdue!!
This guy sells malegeni ku ma security companies for the guards to use during night patrols. Amzake amayima nawo along Kamuzu central hospital – Nature sanctuary road. Propaganda basi!
Aakeera galimoto yopita ku ma deomostratione serious
You do not conceal items for sale you stupid fuck! Plus legeni sagulitsa ndi ma nut and miyala yomwe. Anthu openga mukuganiza bwanji? Admit that ku ma demo ena you have your own agenda.
I really believe the poor guy was eying a lucrative business of selling these deadly weapons at the demos, rather than using them himself. Either way he’s probably the most stupid of the demonstrators.
Is this a serious security issue? I have seen a lot of people carrying and selling catapults in town, how many were arrested? Is it a coincidence that we had HRDC led-demonstrations that’s why the poor man is arrested?
What about those who try to bribe our judges at the ConCourt, are they going to be arrested kapena ayi?
This is putting things upside down. Leave the poor man so that he sells all catapults PLUS stones. He only wants to feed his family, period.
Ife amene takulira kumudzi, legeni imayenda miyala limodzi for it to be usable. Palibe nkhani apa. Leave him. M’malo mogwira milamba ndi nsomba zikulu-zikulu, mukugwira matemba okha-okha bwanji?
Masiku ano, catapults are used by security guards and other security personnel but in the village, people use it for killing birds, snakes, etc.
This is an obvious propaganda, amutuma anthu wosafunila dziko zabwino kuti atenga zida kenaka amugwire aziti ndi wa HRDC wofuna zaupandu…….palibeeeeeee…………..more fire HRDC! Malawi asinthe basi……….
Vuto la anthu a nyau simufuna kuvomereza mukalakwitsa!
Agwidwawo amangidwe basi ndi awo omwe amenewo ife tayenda bwino popita ku ma demo sitikwera minibus. Timayenda zamadulira
lethal weapon is the dicks of those police officers shamelessly raping girls in uniform like its war torn DRC! And still walking scot free and having the audacity to quickly arrest Jessie and Timonty and friends over the girlfriend termirk story but not these officers that raped and abused people in Nsundwe. Selective justice cover up…..all must face the law equally and been given a chance to appear before the court for self defence.
What of your own dick idiot? Legeni is the symbol of your foolish boss Zeze Arafat. Mwagwa nayo lero abakha inu.
You are just one pathetic idiot who cannot face reality as it is. So to you it was better for this beast to vandalise property and kill innocent souls in the name of “peaceful demonstrations”. You truly know that the Nsundwe rape issue is just a cooked up story by HRDC and some wasted brains like yourself. With this greed you will allow thieves to rule this country forever. We surely need change but with this approach of yours, I would rather go for the devil I know. Wise up people and be the true change we are looking for, not this savagery
Nanaga poti mipeni ndi malegeniwo amapita nawo kogulitsa, mwa nthawi zonse. Mutayeni ndi business yake iyi. Kagwileni wochita bribe ma judge osati wpnyamula malegeni.
Zopusa!
What did the idiot confess? Amagulitsa ma legen ndi machaka ndi miyala ndi ma nut omwe? Ask Arafat Hamdan the Boko Haram leader like this ugly Mtambo
Like thieves ruling now.
@Patrot, you are a die hard cadet. everyone here knows about that. Unasowatu pakatipa pa forum pano. Welcome back.
No insults please good Malawians ngakhale muli okwiya osatukwanana