Thugs ‘shoot-to-kill’ Malawi Police officer, arrested: Updated
Malawi Police managed to arrest a gang of suspected robbers who shot dead a police officer who was in a minibus of a Petroda Filling Station in Lilongwe and robbed bags containing cash.


Thugs are reported to have ambushed a Petroda minibus at Chilambula Road after it had just left the filling station to bank millions of Kwacha.
They fatally shot at a police officer before robbing the cash.
Police Public Relations officer, Rhoda Manjolo said Police have launched investigations into murder.
Eye witnesses say the robbers who were using a black sedan without a number plate dumped the vehicle at Chitukuko in Area 15.
On Sunday thugs shot a UDF director of youth Ibrahim Maloni in Area 47 where they went away with cash and other valuables.
Gun crime is on the rise in Malawi.
Meanwhile, Police say armed robbers who killed a police officerand driver of a minibus belonging to Petroda Ltd have been caught.
Follow and Subscribe Nyasa TV :
Malawi Police Show Ur Action As Real Professionals In Ur Work.
Koma ine ndimadabwa kt apolice mumatha kudziwitsidwa kt apa paliokuba in mumadikila aphedwe munthu ngati mmene zachitikiramu.Enanso ali pa Mbayani pazikwanje mucilage wapolice amuphe kenako mukakhazikise chitetezo
R I p.
Where are our Human Rights Organisations this time? Who has got the right to life the killer or the one who is killed. Here the life of an innocent policeman is gone and you learned people claim that the life of the criminal should be spared because he has the right to life. What a nosenses Ndalama a Malawi zatisokoneza makhalidwe ndi maganizo.
onyaata omwe otha’xeno omeewa!
onyamata omwe othawa xeno omeewa!
Ndiye mukagwira mbamvazo chonde muziyesetsa kuliziwisa dziko mwatchutchutchu kuti tizizisata bwinobwino.
ngati mtengo wauwisi ukupsa whatabout ouma may the soul of police officer rest in peace
Up to gun point takagwireni ntchito abale
Lamulo lakupha boma libwereseredwe, This caprits need to be hanged in public. I am sure all these thieves wil disappear. Bt if you lock them up at one point they will be pardoned , and will be back on scene to accomplish there mission.
akubawa tamawaphani please,tatopa ndikumva za imfa za anthu achitetezo.anyapapiwa mukawagwila mumawamanga zaka zochepa,penaso mumawasiya mukanyemelana dorobucci.sizilibwino police say no to corruption to improve security measures.
I can kip my mouth shut on this: Thats a good sign,. telling us our security is breached. The Government has to do something on this. Mwang waini wake wapita,mwina anali ndi chibonga chokha ndi mahand caff.Zoopsa.
Chinachitika ndi chiyani wachitetezo kukweranso the same vehicle momwe munali cash bwanji sanagwiritse galimoto ina ndikumairondola min bus? Komanso a Group 4 mumawakaikira? RIP
When you dethrone love and righteousness in your heart carnality and chaos get crowned. May the lord help Malawi! May the Lord comfort all those affected by our dear son’s death.
Koma umunthu wanu ulipati akuba inu. Zoona ndalama za eni mpaka ku shooter minibus ngati kunkhondo kuli kufuna kutenga zaweni? Almighty father in heaven.. we call upon you to heal our land. Patokha talephera
It’s about robbery, corruption, defilement, sexual cases, climte change, unemployment rate rising ,xenophobia,hunger, earthquakes, all over the world,what does it tell us? Jesus is coming .are we ready? Be honest in your response.
Bab news 4 malawian may his soul RIP.
Who are they, let all Malawians know their names and let justice take its course. Otherwise … If identity of these thieves is withheld the credibility of security agencies will be doubted.
Ulova wakula malawi; boma lisapitilize kukhuwimisa zithu; ku mapasport ku madriving laicence; zinthunzi zinakwera kwambiri, athu ambiri ndiosowa pogwira choncho amadalira kupeza pasport or driving laincence; choncho umbanda siutha.
pliz boma ikani chitetezo chokwanila kwa apolice ateteze ife komanso iwo ateteze moyo wawo
Police Officers are our own sons and brothers, they are not our enemies. Please let us love and appreciate them. Without them even the own parents could have been long gone. Most of them live very pathetic lives. Why are they being killed for money they do not own please let us consider the families that are bereaved of a father a son a brother. God is watching us.
Nice that they are finally caught. Lets law takes its course. RIP police dead
Akapusa azikwapulidwa choncho
masiku omaliza police R I P!
Everytym ndimaona maganizo a anthu pa nyasatimes,amakhala mcp kulimbana ndi Dpp n alhomwe,listen up zimenezo sizingathandize..we need to hv one sprit ngat a malawi.only that titukula dziko lathu.osutsa boma learn to work with government and automaticaly zolephera zaboma zizikonzeka in progress thereby tipanga progres,,,dnt blame apolisi kut ndiakuba ayi..wina aliyense ndiwakuba.kutenga chaeni popanda chilolezo that is.ndiye ndizingat mwatenga popanda eni ake kudziwa? Zambir.cashgate inayamba kale even tym ya yesu.anthu okhometsa tsonkho and mu buku la lopatulika pa chiphunzitso cha yohane mupezanso uthenga wake…
Root ya nyasi zonse kumalawi ndi chifukwa choti chikondi tilibe….tipemphe ambuye atipatse chikondi kut tinthe kukhala mwamtendere.with love,there is no wamkulu(kuzikweza),cashgate(kuba),shoot to kil(kuphana),kutukwanizana,kugawanikana(fedelism)…mzako akakhala pamavuto umayenereka umuthandize kaye then umuzuzule pambuyo….pepani anamfedwa,mulungu ndiye mwini moyo,akudalitseni,akutothozeni.nonse mwatukwanidwa khululukani..zikomo
Ngati agwidwa let their names be known so that their friends are caught and brought to book. anthu a community akuwadziwa chonde tiuzeni mayina awo kwinanso kuti anthu achenjele poyenda. The community will give you the other names only if the names of these thugs are released. Parade them on TVM and all media houses so that we take care next. Osawasiya ndithu lets deal with them. This is becoming unbearing.
Jesus is coming soon. How can you do that to your fellow countryman. Opanda mzimu anthuni bwanji? Shame on you ndithu. Koma dziwani kuti mudzayankha ndithu very soon.
We nganya,
munthu sanganiza za moyo wamzake chifukwa cha ndalama. EEEh! ndaonela Raph kodi ndalamazo uzidya bwanji brain ili affected ndi maganizo akuti ndapha munthu?
RIP, Policeman – bola a Boma azipereka compensation kwa ana kapena makolo.
KILL THEM TOO.
iwe no. 124, ndiwe chitsiru, lero akuba abwere kunyumba kwako, akukhapekhape, usakapite ku polisi poti ukuti apolisiwo akadaphedwa. izi zikuchitikire ndithu
owo!! zavuta coz wa plice waomberedwa. ndipo ndikanakondwa akanamupha. m’mayesa wapolisi ndiye wakubayo. wapolisi yemwe anatiber ku chilobwe siuyo ali ku chikwawa police. sanamuchotse nchito koma nanakamubisa ku chikwawa, ati kumuuza kuti usamaonekera ku blantyre. zopusa
Ayeni ndalama sanasate njira yoyenera yotengera ndalama pa galimoto. Akanagwirisa nchito open vehicl asilikaliwo pa mwamba pa body. Nhawi yomwe anawachinga nthawi yomweyo akanalumpha nawo chipolopolo kugwa pansi kuchita mannorver mkati mwa galimoto uwomba bwanji mfuti?
ma suspect oyamba, kawagwireni ku petroda.mfiti ina ikudzawapo kanthu kumeneko.mudzafa imfa yowawa mukamaphetsa anzanu pa ncthito mu dzina lofuna ndalama zosavutikira
Thats not fair, company zotele zithandizenso banja la malemu especially the little ones who have a long way to go, those people get very little allowance yet has died to save ur billions
Anthu amenewa ngati agwidwadi aphedwe basi,pasakhalenso za maufulu apa,owona zamaufulunu,waphedwayo atakhala mwana wanu,wakuphayo angakhale ndi ufulu kodi? ngati simukwanitsa bwera naoni poyela ice ngati mob tikhoza kuchitanawo.
Thats shoot to kill for you, ma robbers pamenepo anatenganso phunziro
Obviously an inside job or tip off by the Petroda staff. Also I hope the diseased was the gun totting 17 year old thug from Area 18 station who was harassing motorists on Wednesday night.
Where do the guns come from? Only the police and army have easy access to weapons, a few come from Moz. So better accountability by the police would be a start to combating armed crime in Malawi.
OKUBAWO AZIPHEDWA BASI
Ngati awagwiradi anthuwo maina awo ali kuti ???
Zaboza zaboza zamanyazi
Cry my beloved country
akapezeka akuphawo anyongedwe.
Tili m’masiku omaliza,Baibulo linalemba kale
sinali galimoto ya black imene yasiidwa pa chitukuko mwanhopanga assume apa simunafunse eyewitness really?? nwae ma NGO atipo bwanji wapolice waphedwa
Ophwanya Ufulu wamnzake nayenso wake Uphwanyidwe!! Ngati agwidwa, Aphedwe basi. Take them to an open ground and SPRAY them with gun bullets anthu onse akuona. Ena atengerepo phunziro.
I FEEL POLICE MUST REFUSE CERTAIN ASSIGNMENTS AFTER RISK ASSESMENTS.THIS COULD BE INSIDE JOB-HOW DID THUGS KNOW CASH WAS TO BE BANKED ON THAT DAY AND THAT TIME?POLICE OFFICERS ON GUARD MUST ALWAYS BE SKEPTICAL OF FUEL ATTENDANTS AS WELL AS VAN DRIVERS.TRUST NO ONE THE LIFE IS YOS
Chala changa!
I think were going in the right direction. Its good that Malawian thugs who for long have been best friends with Malawian police officers in terrorising innocent civilians have now turned their guns against the police themselves. This is a welcome development. I sincerely pray that when they are done with the police, the thugs should also turn the guns against their next best friend; lawyers who bail them out after killing innocent people. Until criminals masquerading as police officers or lawyers understand that criminals are bad citizens and do not deserve our protection, we shall be having problems with crime. Well done criminals this far, teach the police what crime is so that they can start taking crime seriously.
Mob justice or shoot to kill that’s the only way to deal with theses thugs!
mapeto azikoli
Eeeish 16 shots without retaliation ndinkhaza zowopsa Mulungu akakulangani muwona.
Gwirani mbava zoopsazo osati wanjinga ya kabanza, please!
killed or slaughtered?
Pitfall tulo. Kodi osaombera overnight millionaire Ben phiri bwa?
ZANYANYA PA NYASA LAND GUYS
ALIYENSE DISO BIIII PA KHOBILI
ZA MANKHWALA MZIPATALA, NDI CHITUKUKO
NDE NJEEEEE
NGATI APHEDWA APOLISI ANTHUFE TINGATANI
Sizandale izi akuba analipo olo nthawi ya kamuzu,umbuli basi
A police gwira ntchito yanu
Bola musamagwire anthu osalakwa ndikumati ndi mbava. Chifukwa ntchito ndiye ikukuvutani.
Bola mudamagwire anthu osalakwa ndikumati ndi mbava. Chifukwa ntchito ndiye ikukuvutani.
nzomwe munavotera
koma zinaz zanyanya iesh!
AKUPHAWO APHEDWE BASI! NGAT NDIUFULU KUWALEKA NDIMOYO,NANGA APHEDWAWO SIANTHU?TICHITEPO KANTHU:
Limeli likhale phunziro kwainu makampani ogwira ntchito za ndalama mumakonda njira zachidule kwambiri muti saving costs look here mwabetsa ndalama,mwaphetsa anthu komanso mwaonongetsa katundu wakampani. Anthuwonso mumawalipira tindalama tochepa yet mukuwasezetsa mamillion thus why akumapanga connive ndi mbavazo. G4S ndiye ntchito yake imeneyo koma mukuti ayi kudula,nanga yapa mwasever ndalàmazo? Kaya, nane ndiri ndianga mavuto obisalira eni dziko kuno(zhenophobia). Pepani mabanja osiyidwa mulungu akutonthozeni munthawi yansautsoyi.
thumbs up ma, I salute u. I really dnt understand these other companies, they alwyz operate in shortcuts. luk nw lyf of someone has been involved. MHSRIP
KILL ALL THUGS olo okuba ingakhale mbale AFE NDITHU.
CAN DPP REINFORCE THE SHOOT TO KILL PLEASE?
Or do they want the mob justice to take over.
Zachipani ndi kuphedwa kwa apolice zikugwirizana? Thawi ya UDF + MCP kunalibe ma robbers? Angopatsidwa za kuombera akuba.
Mashaalah my alah bles the family of desesead amen??
Its high time these Indians should learn to use safe means of getting cash to the bank I.e. Using G4S cash transit. How many times have these people been robbed while taking cash to the bank? Remember Citymall issue.
If they have been caught already then excellent job by the police. I’ve always wondered however how our cops never fire back during these incidents, is it they are ill equipped, poorly trained or not alert to see the danger approaching?
Zanga phe @ 66 its deceased not diseased … koma alomwe?! Go to xul pls eeishhh!!
Inu a Bamusi C. Phiri ndikugwirizana ndi mfundo mwanenayo.
We will provide security to investors.
Abale tizikhalura kulira masikuwa Army pofunika alowerere monga ziriri kuno Ku R.S.A. Koma anthufe tizithandiza apolis kugwira ntchito yawo.
Mwaba mwagwidwa akaphedwe muwadyetse cement sizodyera kundende Ndalama za msonkho zathu shupit
Where were the armed policemen at chipiku doing when guns were toting at the scene of crime which is just yards away . Many questions than answers . This must must have a sophisticated syndicate . May the soul of our departed policeman rest in peace .
This is unacceptable the police must use all the resources available to get to the root of all this. What is the so called CID guys doing cos this needs investigations. These must be stopped henceforth. Don’t politicise this but come along together to deal with this. Kiliing police officers? What about civilians, if thugs cannot respect police officers??????
One day zonse zizayenda pepani mabanja mwakhuzidwa ndimoyo waanthu achifwambawa mulungu timenyereni nkhondo
One day zones zizayenda pepani mabanja mwakhuzidwa ndimoyo waanthu achifwambawa mulungu timenyereni nkhondo
This Iz Bad. May God Hav Mercy On Them!Kukonda Ndalama Kwa Mtundu Wanji Mpaka Kulimba Mtima Kupha Munthu. May The Soul Of The Police Man Rest In Eternal Peace.
Its very pathetic how our security is handled with security agents. Look at NIB the so called National Intelligence Bureau which is operating illegally without an Act but gets big funding just for political which hunt. Instead of helping Police with the intelligence they need to combat come. MP ‘s must agree to dissolve this political influenced organisation and empower the Police with the money being given to this bureau to help police officers secure informants. Pls lets not loose police officers in this way
And here we have stupid clueless and inept leaders like APm running around telling donors it is safe to invest in Malawi. This is anarchy!! The president as commander in chief should put policies in place. For example go to parliament and introduce new laws against serious crimes. A minimum of 30 years with hard labor for any one caught in a robbery. Try it and see! you will cut this foolishness in half. It is not rocket science to note the causes of this type of behavior. People are getting away with murder without serious consequences. We did not have this during Kamuzu its only after these corrupt and greedy idiots came to power. I wish some one would terrorize his family may be thats when he will do something sensible. Mediocrity leadership kudziwa kuba basi
Iwe no.:25 kaya ukuti ndiwe Tembusha ndiwe opanda nzeru, moti MCP ndimavuto achitikawa zikugwirizana bwanji? Mukasowa zolemba ndibwino kumakavina Tchopa ndi a Mbuyako upanda manuwo shupit.
Every time we hear of robbery especially those involving police, we hear tragedies that one police officer has been shot dead. About civilians is not my subject today. Do you have people in police doing researches that may improve service delivery? Our dear president was reminding academists of this, and this message goes to every one including you security service providers. They are able to know times and places where to robe money, they plan for their travel, no. Of bullets to load, time frame for the operation. Eg. Sending one police officer with one gun against unknown number of thugs. If this one gets shot? G4s can not be the best over our trained officers. Traffic police are usually more than three asking license and check for insurance and COF, just to mention a few. Sleeping dogs.
Wakuba sangadziwe pa iye yekha za ndalama.nkhani ndiyakuti pa petrodapo pali satana winawake amene anapeleka information kwa akuba.koma ali ndi tsoka waphetsa anthu osalakwa.ndalama za kaisala izi tizisia pompano pa dziko
DPP thugs imeneyi
To His Name Be De Glory.R I P
Hahahaha DPP chitetezo!
Why is it that our police men/women are treating these heartless people with kids gloves? Shoot to kill must be enforced by our police men and people should continue burning them whenever they are caught. I don’t know if these people were made in the image of God.
Zayang’ana kungolo,chifukwa waphedwa ndiwapolisi ndiye mpakana press briefing,akadakhala mlimi zidakatele?
C.C.TVs must be mounted to all filling station please, those are sensitive places,i wonder why only one officer on duty at that time you won’t see a robber coming single they come in large numbers and they play do or die game.So Commissioner of police please don’t let this happen again put two or three officers at a station please.
If it was an army officer i would not worry because they feel themselves on top of everything,they end up bulling our local people for nothing.But they don’t reach such extent so any ways.Sorry to the diseased i am really shocked.See my name.
Lord have mercy.
Zonse angoyang ana yawe RIP………..
Sad news, tiyeni tithandize kufufuza mbavazi anthuwa ndi oipa,
Propaganda ya MCP ndi PP imeneyi kuti adziti Boma larephera
Shame on these parties
Sorry, Our Lord may you comfort the family
Ahaaaa! Nanunso ndalama amakwedza minibus popita ku bank? Kkkkkk ndiye mudzionatu!
THIZ ARE DPP THUGS WHO KILLED CHASOWA
PUT THEM DOWN NO COURT
THEY WILL GIVE THEM BAIL
Fanz choti muziwa pankhani yobedwa ndalama imachokera kwa ogwira ntchito chifukwa ndiamene amadziwa information ndipo choti mudziwe ogwira ntchito ma petroda ndi akumwera ndiye choti mudziwe mbava zambiri ndizakumwera,kuyambira mapulenzident onse akuba ndiye ana nawo mumati atani?ndipo wafayo wafera ntchito zotsatira za ntchito ya security ndi ifa and is very dangerous.RIP.
Whether it is inside job or not, true speaking Malawi is a failed state. Crime and also corruption is very high in our beautiful country because of unemployment. Lack of opportunities in Malawi also poverty and hunger these are main cause of crime in our country. Government must fight crime by giving its citizens opportunities and decent jobs. ‘Shoot to kill’ will not solve anything.
Kill them now, don’t wast time going to court with these dogs.
Akapezeka amenewo muwaphe basi
To all those who are saying Petroda should have hired G4S are you trying to tell us that we have more faith in a foreign based securical company than our own Malawi Police ? Let us mourn our lost friends and pray for those who were injured physically and mentally and not point our dirty fingers instead of criticizing and wishing how things could be otherwise. It is what it is.
R.I.P
RIP
Chondiwawa nchakuti anthu osalakwa akutaya miyoyo yawo mukagwiranso mbavazo zikumatuluka pa bail zikatelo milandu yake siyiziwika komwe imakathera komanso ku malawi kulibe shop yogulitsa mfuti fufuzani mfuti zikuchoka kuti kale zoterezi zimasowa kalangaaa ine malawi wa lero
A president chonde pagani izo akulu anu anachita. Shoot to kill BAMA ZONSE.
RIP. How many were wounded in the minibus?
Mbavazi ndi za DPP disgruntled with little cash from their master, Peter Mutharika. Shame on DPP
mhrinp
Please Police provide bullet proof attires to our I’ll equipped police. We are tired of these reports of our officers killed like chickens while on duty.
I saw him down in hopelessness after the brutal attack, may GOD have mercy upon his soul and his family.
The “warm heart of Africa” indeed.
mukulimbana ndi anthu omwe akukutetezani chifukwa chiani?muzikapha azibambo aja akumanyamula mahule(boko haram )usi.amangoti zungulizunguli ngati ma sipokosi mtaunimu,kupusa tatopananu akuba
Akuti wakubayo zina lache ndi Robert Harawa!
Mwaonatu atumbuka vuto lanu, Mukufuna kuti anthu aziti ndi DPP.
oh my his saul rest in peace gvt why why human rights why see thugs do to officers apa kumati wakuba ali ndi ufulu mwina timva inu a human rights coz mumakondwa akuba akamapha apolice chonchi akadakhala wapolice kupha sibwezi mukumuimba mlandu wakupha apa zimenezi kuba kotereku sikungathe ngati a human rights ndi mutasitha mfundo zanu pa anthu akuba wakuba amakhala ndi ufulu bola shariya itha kuthandizapo
The problem in Malawi is that we dont have a leader, uyu pitala is too old and he is not in control
MUCH THAT WE KNOW POLICE SERVICE IS FOR INTERNAL SECURITY, PEACE, ETC, AT THIS POINT IT IS BECOMING UNBEARABLE.
WHAT IS NEEDED IS PEACE NOT TODAY TOMMORROW CITIZENS BEING SHOT LIKE CHICKENS.
SOLDIERS CUD ALSO JOIN THIS CRITICAL TIME THAN INNOCENT LIVES BEING LOST LIKE THAT UNTIL SUCH A TIME
May His Soul Rest In Peace and may the good Lord comfort the bereaved family.
When will this war of cabbing out criminals be won? Innocent lives police officers are time and again are being lost by these people. I feel pity when i see Traffic Police officers receiving spot fines without an armed officer around. At least when conducting their jobs (traffic) one should have any type of a gun especially revolvers. It is high time we change our mind set in police on the fire arms act. Issuing everyone of them its good yes but will they serve the intended purpose? Bullet vests are a must to everyone more especially those tactical type from MARS model 55, 83 etc not just giving this one and that one not. Are these people who are on private jobs like the one above insured? Don’t think of how much we will loose but how many lives we will save.
REQUIESCAT IN PACE ” REST IN PEACE)
a human rights lankhulaniko paja mubakira mbava. apolice akuphedwa simukulankhulako muli moyo?
An eye for an eye would help
SO BAD
The opening sentence says police are hunting for thugs then the last paragraph says the thugs have been caught……..
Malawi m’masiku otsiliza..
Is this democracy?No rule of law, security for citizens and property.. Too much lip service.Dziko laono ngeka.Boma liri kuti?
A Ndanga is this politics? Ask Billy
A Ndanga is this politics?
Ambuye muapatse anthu akufa chiusiro chosatha ndipo kuyera kosatha kuwalitse maso awo amen.
Abale ndalama ndiyoyipa mpaka kupha munthu osalakwa. MHSRIP.
Rest in peace
These thugs ndi a MCP! Ndi aja amamenya ku msonkhano wao aja!
Shame on MCP.
This is a tragic loss to the family and nation. Very disheartening and evil. Almighty God see us through and remember this family in these trying times. MHSRIP.
Human rights and foolish lawyers are defending them
Mulangika choncho mukamalimbana ndi munthu wa mulungune. Kkkkkkkk.
May his innocent soul rest in peace !!!
Malawi wanunkha bola kale
………………………..
Bola MCP, PP or UDF
but not this D-PHI-PHI
A Dausi, what is your job really?? mukungosakaza ndalama zaboma basi
Nkhani iyi muyione bwino alipo winawake waku petroda amene anagwirizana ndiakubawo. komanso nditchifuwachani munagwiritsa ntchito min bus instead of G4. Mukutipweteketsera a police amene aliosalakwa. koma khaleni khaleni amene apanga izi apezeka Mdzina la yesu. Rest in peace.
RIP
hey this very bad in comercial center like this please security should be intensified in ll because this is very bad
may his soul rest in peace … the defender of the nations
That’s the problem with most Asians. They do not want to spend money on cash transit companies like G4s but instead use regualr vehicles and then hore a PMF guys to pay the police peanuts. That has cost the life of one father, brother or uncle to someone plus the cash is gone. Inside job.
Malawi walero – Shoot to kill at its best.
May his soul rest in peace, koma ma contract ogadira ndalamawa akutithera apolice ndithu !!
Is my prayer that these thugs should apprehended as soon as possible coz it destroys our good image of peace and stability
Shoot to kill is the way to go if we are to end armed robery
This an inside mission please investgate.
Why did you take min bus instead of G4 security vehicle.
@Jay z..very stupid and irresponsible comment we are talking about a life here someones brother,father and husband. It only takes a sick minided idiot like you to create jokes!!!
Government should arm every police officer with pistols and bullet proof vests.gone are the days of using those old rifles.please govnt lets arm and retrain our police officers in combat and keep them physically fit and motivate them by increasing their perks.
I agree with you.But many of these police officers too much drinking.Choncho angagwire mfuti ndikuomba? Azingonjenjemera kaya.
Boma illlllo
People pliz mind ur words whn commenting
‘
Tidapuma zamfutizi nthawi ya amayi,tikangomva za Cashgate koma DPP yabweranso ndi yao ija.
Once upon a time in Malawi, one person was talking to investors to come to Malawi while his counterpart was chasing the same investors out of Malawi.
MHSRIP
Chitetezo mmalawi muno mulibe komaso apolice athu amayenda opanda mfuti choncho angathane bwanji ndi mbava
The country has gone to the dogs.
We thugz u not gonna finish us moti mawa tikukaba ku state house
Boma la DPP limenelo